26/09/2023
TIZISAMALA NDI MALOTO OMWE TIMALOTA
Maloto ali magulu angapo ndipo umayenela uzindikile kusiyana kwa maloto amene umalota
Maloto ena amabwela chifukwa cha kuchiganizila kwambili chinthu ndipo maloto awa amakhala opanda tsogolo lililonse
Kulota ukuthamangisidwa koma osagwidwa, ukuoloka pa mulantho wa ntengo umodzi, ukudupha zenje, kapena ukuuluka malele, Imakhala khondo yomwe ikuchitika pamoyo wanu kuchoka kumidima ndipo Yehova akuoneselani ndi kukuululilani kuti akukumenyelani nkhondo ngakhale mukugona,
ndipo chomwe chimafunika ndi kudzuka ndi kupemphera kumuthokoza AMBUYE
Kulota zithu zoopysa monga ukumenyedwa, kapena uli matope ukukanika kutulukamo, penaso kumalota ukubanika mwina kumafuna kuti udzuke koma kumakanika, kulota zinyama zoopysa kapena malilo
Okondedwa iyi ndi khondo yoopysa ndipo ukapasidwa mwayi ozuka yamika Kumwamba chifukwa ambiri omwe amafela kutulo amakhala wakumana ndi khondo ngati izi, Ndipo izi zimachitika kwambiri pamene wagona osapephera "Nkhaniyi ndiyoonadi ndithu"
Kulota ukupha somba, ukukumba m'tedza ochuluka kapena ukukolola mbewu zimaimilila tsogolo lowala ndipo ukapephera patalike pafupike umazafikila ku chipambano ndi kulandila zomwe ziri zako
Kulota malilo matenda kapena kutha kwa ntchito ndipo pamapeto pake ndikuchitikadi, maloto awa ndi a uneneli ndipo samantchedwaso maloto ayi koma maso phenya ndipo zindikila kuti mwa iwe muli m'zimu wa uneneli ndipo ukakhulupilika posala kudya ndikupemphera m'phaso iyi imazaonekela pa iwe
Chofunika kuchita👉pamene mwalota zithu izi pinda bondo pempherani kususana ndi ma plan asatana pa moyo wa muthu yemwe mwamulotayo ndipo kukacha kamuuzeni kuti azipemphera kwambiri chifukwa wazungulilidwa ndi nkhondo
Kulota ukugonedwa kapena kugonana ndi munthu,
Pansi pa nyanja pali azimayi ndi azimuna omwe amakugona kumaloto ndipo akamakugona iwe umamva bwino mpaka pena kufika poziipisila, amakuoneselani nkhope ya m'kazi kapena mamuna wabwino cholinga ukomedwe ndipo amatenga m'phamvu yako nkupita