Association of Catholic Journalists - ACJ in Malawi

Association of Catholic Journalists - ACJ in Malawi The ACJ is a body whose membership is
drawn from Catholic journalists and communications personnel.

10/05/2026

Kanema woonetsa momwe zinaliri ku m'mawaku pomwe nthumwi ya a Papa m'maiko a Zambia ndi Malawi Archbishop Gian Luca Perici anatsogolera Nsembe ya Ukaristia ku St. Augustine Cathedral m'dayosizi ya Mangochi.

Nthumwi ya a Papa yoyimira mayiko a Malawi ndi Zambia, Archbishop Gian Luca Perici, lero iri ku St. Augustine Cathedral ...
10/05/2026

Nthumwi ya a Papa yoyimira mayiko a Malawi ndi Zambia, Archbishop Gian Luca Perici, lero iri ku St. Augustine Cathedral m'dayosizi ya Mangochi.

Ku m'mawaku ‎Archbishop Perici watsogolera Nsembe ya Ukaristia pomwenso panali Ambuye Montfort Stima, Vicar General bambo Davie Mambo komanso ansembe ena.

‎Archbishop Perici acheza m'dayosiziyi masiku anayi, ndipo panthawiyi akhala akuchita misonkhano ndi atumiki a Mulungu, akhristu eni ake komanso kuyendera zina mwa ntchito zomwe dayosiziyi ikugwira.


https://www.facebook.com/share/19pCdA1SzF/
20/03/2026

https://www.facebook.com/share/19pCdA1SzF/



Straight from a 7am Mass officiated at Bvumbwe Parish by Rev Fathers Louis Tsuro and Petro Chilumpha, praying for God's travel mercies, representatives of the Catholic Men Association (CMA) in Thyolo and Bangwe deaneries in the Archdiocese of Blantyre have this morning left for St. Andrew Kaggwa Parish in the Lilongwe Archdiocese.

It is all to join their counterparts from other deaneries from Blantyre and all eight dioceses in the country for the Third CMA National Annual General Conference.

The three-day gathering, which starts this evening, is being held under the theme "Rooted in Christ, CMA members sent as agents of evangrlisation'.
In his homily, at Bvumbwe Parish, Father Tsuro, who is the Thyolo Deanery CMA chaplain asked the CMA members to use the general conference to help them deepen their faith and, also, become more responsible in caring for their families.

A programme released by organisers of the event indicates that the conference will start this evening with a recollection on the theme while Right Rev Bishop Vincent Mwakhwawa will tomorrow preside over the Eucharistic celebration which will mark the opening of the conference.

The programme for tomorrow [Saturday] includes presentations on Mental and Prostrate Health, Implementation Phase of the Synod and Pathways towards Synodality, Catholic Men and Family, CMA Strategic Plan, and Church position on Human Trafficking, and the day will end with a cultural night.

(Report by Michael Mmeya)

https://www.facebook.com/share/p/1Fcd9seiH2/
11/03/2026

https://www.facebook.com/share/p/1Fcd9seiH2/

Papa Leo wasankha Dr. Vera Songwe wa m'dziko la Cameroon kukhala membala wa sukulu ya pamwamba ya ku Vatican yotchedwa Pontifical Academy of Social Sciences (PASS).

Dr. Songwe omwe ndi katswiri pa nkhani za chuma ndi ndale malinga ndi maphunziro awo ku sukulu za ukachenjede zosiyana-siyana anabadwa pa 31 August m'chaka cha 1968.

Mwa zina kuyambira m'chaka cha 1998 mpaka 2015 iwo anagwirapo ntchito ku World Bank komanso kuyambira m'chaka cha 2017 mpaka 2022 anagwirapo ntchito ku bungwe la United Nations ngati wachiwiri kwa mlembi wamkulu wa bungwe la United Nations.

Sukulu ya pamwamba ya Pontifical Academy of Social Sciences imachita kafukufuku pa nkhani za chuma, moyo wa anthu wa tsiku ndi tsiku ndi chikhalidwe chao, malamulo ndi ndale ndipo kafukufukuyu amathandiza Mpingo pa zomwe umaphunzitsa zokhudza moyo wa anthu.

The Eastern Chapter of the Association of Catholic Journalists (ACJ) has today planted 150 trees at Diada Primary School...
11/03/2026

The Eastern Chapter of the Association of Catholic Journalists (ACJ) has today planted 150 trees at Diada Primary School in Mkwanda Village, under Traditional Authority Chimwala in Mangochi District.

Head teacher John Andrew Phiri thanked the journalists for the initiative, noting that the school previously had no trees on its premises.

Phiri said the school will work together with surrounding community members to ensure that the trees are well taken care of.

Speaking during the exercise, ACJ National Secretary General Western Guta said the tree-planting activity at the school is part of promoting the message of the late Pope Francis, who demands urgent action against global warming, waste, and pollution, highlighting that environmental degradation disproportionately harms the poor.

Giada Primary School opened in January 2025 and currently has over 200 learners in Standards 1, 2, and 3.

Mwambo wokonzekera chaka cha mayitanidwe mu Mpingo wa Katolika m'dziko lino pansi pa bungwe la Aepiskopi la Malawi Confe...
09/03/2026

Mwambo wokonzekera chaka cha mayitanidwe mu Mpingo wa Katolika m'dziko lino pansi pa bungwe la Aepiskopi la Malawi Conference of Catholic Bishops (MCCB), kudzera ku bungwe la a Papa la Pontifical Mission Societies (PMS Malawi), watha ku Mangochi Cathedral.

Mwambo wa lero amakhazikitsa chikondwerero cha mayitanidwechi, chomwe chidzachitike Lamulungu pa 26 April pa dziko lonse, ndipo kuno ku Malawi chidzachikira pa Mangochi Cathedral.

Dayosizi zina zomwe zikuchita mwambo ngati womwewu lero ndi za Zomba ndi Mzuzu, pomwe Arkdayosizi za Blantyre ndi Lilongwe komanso dayosizi za Dedza ndi Chikwawa zidzakhazikitsa Lamulungu likubwerali pa 15 March. Dayosizi ya Karonga idzakhazikitsa pa 29 March.

M'mawu ake, Bishop Montfort Sitima yemwe amatsogolera mwambowu, walimbikitsa achinyamata kudzipereka kukatumikira ku unsembe, usisiteri, ubulazala ndi moyo wa banja, ndipo omwe anadzipereka nawo apitirire kudzipereka chimodzimodzi.

Komabe, Bishop Sitima wadandaula kuti achinyamata akumamva msanga kuyitanidwa ku banja kokha, kulekana ndi unsembe kapena usisiteri, komanso pali kuganiza kolakwika kuti oyitanidwa ndi a ku sekondare okha, osati ku yunivesite, motero wawalimbikitsa kuti onse ali oyitanidwa.

Dayosizi ya Mpingo wa Katolika ya Mangochi lero ikutsogolera mwambo wokhazikitsa zokonzekera za tsiku lopemphelera mayit...
08/03/2026

Dayosizi ya Mpingo wa Katolika ya Mangochi lero ikutsogolera mwambo wokhazikitsa zokonzekera za tsiku lopemphelera mayitanidwe mu Mpingowu.

Dayosiziyi ikulandira udindo wofalitsa za mayitanidwe m'chakachi kuchokera ku Arkidayosizi ya Blantyre yomwe yakhala ikutsogolera ntchitoyi mchaka chapitachi.

Padakali pano, mwambo wopereka zizindikiro za udindowu wachitika pomwe nthumwi zoyimira achinyamata ku Arkidayosizi ya Blantyre zapereka kolona komanso kandulo kwa Ambuye Montfort Sitima wa Dayosizi ya Mangochi omwenso atsogolera mwambo wa Nsembe ya Misa.

Malingana ndi Ambuye Sitima, kwa nthawi yaitali achinyamata akhala akuyimba nyimbo ya mayitanidwe koma osayankha ndipo alimbikitsa achinyamatawa kuti nthawi yakwana kuti azivomera kuyitana kwa Mulungu.

Anati Malembo Oyera amanena kuti "Munda wakula koma antchito ndi operewera".

Mpingo wa Katolika umayitana achinyamata ku utumiki kudzera mu unsembe, ubulazala komanso usisiteri.

Address

Catholic Secretariat, Area 11, P. O. Box 30384 Capital City, Lilongwe 3
Lilongwe

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Association of Catholic Journalists - ACJ in Malawi posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share

Category