Congress Church

Congress Church Mbewe wa Dzalanyama ndi liwu la Isaiah Emmanuel Sunganimoyo yemwe amayankhula pa nkhani za ndale, zipembedzo, uzimu, chikhalidwe ndi mbiri ya anthu.

06/06/2026
Next President of the Malawi Congress Party (MCP) after Dr. Lazarus McCarthy Chakwera in 2040. Wina atsutse tione!
06/06/2026

Next President of the Malawi Congress Party (MCP) after Dr. Lazarus McCarthy Chakwera in 2040. Wina atsutse tione!

Mchewa ndi Mchewa basi, sangasinthe mawanga ake. Mbewe wa Dzalanyama ndi Nyama Zake mu 2020.
06/06/2026

Mchewa ndi Mchewa basi, sangasinthe mawanga ake. Mbewe wa Dzalanyama ndi Nyama Zake mu 2020.

04/06/2026

Pa 7 June 2026 ndidzayankhulapo pa nkhani yomwe McFarlane Mgwirinji wayankhula, izi ndiyankhula kutsatira pa zomwe iyeyo adanena tili ku Maula Prison. Mudzakhale pomwepo.

04/06/2026

Program yotsatira ndi ya nyimbo za ku khosi kwanu. Kwina tikhala tikucheza za nkhani za ku ndende. Kodi moyo wa ku ndende ndi wotani? Kodi amagonana amuna okha okha monga timamvera? From 1pm to pm. 0999806870

04/06/2026

Kodi moyo wa ku ndende ndi wotani? Kodi amagonana amuna okha okha monga timamvera?

04/06/2026

Program ya lero Tikamba Zomwe yayankhula mfumu Ina ya ku Nsanje. Zikuonetsa kuti Amalawi cheni cheni chomwe timafuna sitimachidziwa.

03/06/2026

Sankhani nyimbo ya ku mtima kwanu tumizani smsku 0999806870 kapena mu comment section, tikhala live pano mpaka 2:15pm. NENANI DZINA LANU, DERA LOMWE MULI. NANGA BOMA MUKULIONA BWANJI?

01/06/2026

Lero tikamba za ku Prison. Maka ndiyankha funso lakuti kumeneko amuna amagonana? Eya ndi zoonadi koma kodi zimakhala motani? Ndipo amagonedwa ndi ndani?

Address

P. O. Box 20131, Kawale
Lilongwe
265

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Congress Church posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share