Malawi na Zambia

Malawi na Zambia Kuchimake kwa Nkhani Zochitika ku Malawi na Zambia mosatengela mbali, Palibe Kubisa kapena Kupsatira.

16/05/2026

1 million kwach or have dinner with Bushiri?

Wapha nzake chifukwa amanenelera kwambiri mtengo wama headset.A fight over a headset turned deadly near  Ngabu Market in...
15/05/2026

Wapha nzake chifukwa amanenelera kwambiri mtengo wama headset.

A fight over a headset turned deadly near Ngabu Market in Nsanje district. A 21-year-old man has been arrested for allegedly stabbing his friend to death.

Nsanje Police say they arrested Steven Reuben, 21, for the murder of 23-year-old Horseback Kambewa. It happened around 11 PM on 14 May 2026 in Matchuwa Village, near Ngabu Market.

According to Nsanje police spokesperson Constable Jabulani Ng'oma, the two were drinking with friends when Kambewa said he wanted to buy Reuben’s headset. They argued about the price, and the argument became a fight.

Ng'oma said Reuben then took out a knife and stabbed Kambewa in the chest. Kambewa walked a short distance before falling down. He was taken to Nsanje District Hospital, where doctors said he died from internal bleeding.

Police went to the scene, collected the body, and arrested Reuben soon after. He is still in custody and will likely appear in court soon on a murder charge.

Both men are from villages under Traditional Authority Ngabu in Nsanje district.

11/05/2026

Ati mphwanga umkafuna kuti uzindidya ineyo?😂

 Apolisi a kwa Ngabu m’boma la Chikwawa amanga anthu atatu pa milandu yokhudza kupha munthu komanso kufalitsa nkhani zom...
10/05/2026


Apolisi a kwa Ngabu m’boma la Chikwawa amanga anthu atatu pa milandu yokhudza kupha munthu komanso kufalitsa nkhani zomwe zingayambitse chisokonezo potsatira mphekesera zakusowa kwa maliseche aamuna.

Malinga ndi mneneri wa polisi ku Chikwawa Sergeant Dickson Matemba anthu omwe amangidwa ndi Thomas Moses wa zaka 31 komanso Montford Tembenuka wa zaka 21 onse ochokera m’mudzi wa Nyaekha mfumu yaikulu Ngabu.

Awiriwa akuganiziridwa kuti adapha Baza Sande wa zaka 34 wa m’mudzi wa Goma mfumu yaikulu Ngabu m’boma la Chikwawa.

A polisi atinso munthu wachitatu yemwe wamangidwa ndi Hudson Thomas wa zaka 26 wa m’mudzi wa Billy mfumu yaikulu Ngabu yemwe akuganiziridwa kuti anafalitsa nkhani yoti munthu wina wamuchotsera maliseche ake.

“Koma titafufuza tidapeza kuti maliseche ake anali bwinobwino ndipo nkhaniyo sinali yoona,” watero Matemba.

Pakadali pano polisi yawonjezera chiwerengero cha apolisi m’dera la Ngabu pofuna kusunga bata ndi chitetezo komanso kupitiriza kumanga anthu ena omwe akukhudzidwa ndi zachiwawazi.

Abambowotu ndi amene analowa ndi phone mu cell aja. Paja simuchedwa kuiwala. Ndi abambo ovuta kwambiri😅
09/05/2026

Abambowotu ndi amene analowa ndi phone mu cell aja. Paja simuchedwa kuiwala. Ndi abambo ovuta kwambiri😅

Amufinya lakumanzele
08/05/2026

Amufinya lakumanzele

Kosaka ndalama sitisankha, koma kodyera. Happy birthday our own content creator, Tupochere
08/05/2026

Kosaka ndalama sitisankha, koma kodyera. Happy birthday our own content creator, Tupochere

07/05/2026

Ana akuti mkuluyi sanachedwe kumwalira. Zoona anamwaliradi?

Anthu ena inu. Anthu ena ake samayenera kuti abadwe ndi manja.
04/05/2026

Anthu ena inu. Anthu ena ake samayenera kuti abadwe ndi manja.

Apolisi ayitanitsa mfumu yamzinda wa Blantyre Isaac Jomo Osman kuti amufunse mafunso pa malipoti oti yamenya mai wina mu...
02/05/2026

Apolisi ayitanitsa mfumu yamzinda wa Blantyre Isaac Jomo Osman kuti amufunse mafunso pa malipoti oti yamenya mai wina mu mzinda wa Blantyre.

Malingana ndi mmodzi mwa apolisi omwe ali pa malowa, pakadali pano Osman akukumana ndi mkulu wa apolisi mdziko muno, Richard Luhanga, mneneri wa apolisi Lael Chimtembo komanso mkulu oona zozenga mlandu kuchigawo chakummwera.

Onelani zonse apa👇👇👇LIVE🔴
https://malawinazambia.blogspot.com/p/breaking-news-margin-0-padding-0-box_23.html

Uli ku family gathering. Nde waona galu wanyambita gawo lake. Waona ndiwe wekha. Ungawauze wena? Be honest..
01/05/2026

Uli ku family gathering. Nde waona galu wanyambita gawo lake. Waona ndiwe wekha. Ungawauze wena? Be honest..

Address

Luwinga
Mzuzu

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Malawi na Zambia posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Malawi na Zambia:

Share